Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 9:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Anawalamula kuti masiku amenewa akhale ochita phwando, kusangalala, kutumizirana chakudya+ ndi kupereka mphatso kwa anthu osauka.+ Anatero pakuti amenewa ndi masiku amene Ayuda anasiya kuvutitsidwa ndi adani awo,+ komanso mwezi umene chisoni chawo chinasintha kukhala chikondwerero ndiponso pamene tsiku lolira+ linasintha kukhala tsiku losangalala.

  • Yesaya 25:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 M’tsiku limenelo munthu adzati: “Taonani! Uyu ndiye Mulungu wathu.+ Chiyembekezo chathu chinali mwa iye+ ndipo iye watipulumutsa.+ Uyu ndi Yehova.+ Chiyembekezo chathu chinali mwa iye. Tiyeni tisangalale ndi kukondwera ndi chipulumutso chochokera kwa iye.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena