Salimo 20:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+ Salimo 21:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Inu Yehova, mfumu ikukondwera mu mphamvu zanu.+Ndipo idzapitiriza kukondwera mu chipulumutso chanu.+ Salimo 62:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 62 Ndithudi, moyo wanga ukuyembekezera Mulungu modekha.+Chipulumutso changa chidzachokera kwa iye.+ Salimo 95:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 95 Bwerani tifuule kwa Yehova mokondwera!+Iye amene ndi Thanthwe la chipulumutso chathu, timufuulire mosangalala chifukwa wapambana.+ Mika 7:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma ine ndidzadikirira Yehova.+ Ndidzayembekezera moleza mtima Mulungu wa chipulumutso changa.+ Mulungu wanga adzandimvera.+ Zefaniya 3:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Fuula mosangalala iwe mwana wamkazi wa Ziyoni! Fuula mokondwera+ iwe Isiraeli! Sangalala ndi kukondwera ndi mtima wonse, iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu!+
5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+
21 Inu Yehova, mfumu ikukondwera mu mphamvu zanu.+Ndipo idzapitiriza kukondwera mu chipulumutso chanu.+
95 Bwerani tifuule kwa Yehova mokondwera!+Iye amene ndi Thanthwe la chipulumutso chathu, timufuulire mosangalala chifukwa wapambana.+
7 Koma ine ndidzadikirira Yehova.+ Ndidzayembekezera moleza mtima Mulungu wa chipulumutso changa.+ Mulungu wanga adzandimvera.+
14 Fuula mosangalala iwe mwana wamkazi wa Ziyoni! Fuula mokondwera+ iwe Isiraeli! Sangalala ndi kukondwera ndi mtima wonse, iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu!+