Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 35:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma moyo wanga ukondwere mwa Yehova.+

      Usangalale chifukwa cha chipulumutso chake.+

  • Salimo 51:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu Mulungu, ndilanditseni ku mlandu wa magazi,+ inu Mulungu wa chipulumutso changa,+

      Kuti lilime langa linene za chilungamo chanu mokondwera.+

  • Salimo 59:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ine, ndidzaimba za mphamvu yanu,+

      M’mawa ndidzanena mosangalala za kukoma mtima kwanu kosatha.+

      Pakuti inu mwakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+

      Ndiponso malo anga othawirako pa nthawi ya masautso.+

  • Luka 1:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Ndipo mzimu wanga sungaleke kusefukira+ ndi chimwemwe mwa Mulungu, Mpulumutsi wanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena