Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 89:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 89 Ndidzaimba mpaka kalekale za ntchito za Yehova zosonyeza kukoma mtima kwake kosatha.+

      Ndidzalengeza ndi pakamwa panga ku mibadwomibadwo za kukhulupirika kwanu.+

  • Salimo 101:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 101 Ndidzaimba za kukoma mtima kwanu kosatha ndi chiweruzo chanu.+

      Inu Yehova, ndidzakuimbirani nyimbo zokutamandani.+

  • Aefeso 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Anatero kuti kukoma mtima kwakukulu kwaulemerero+ kumene anatisonyeza kudzera mwa wokondedwa wake+ kutamandike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena