Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Mukapanda kumvera mawu a Yehova Mulungu wanu ndi kuonetsetsa kuti mukutsatira malamulo ake onse ndi mfundo zake zimene ndikukupatsani lero, matemberero otsatirawa adzakugwerani ndi kukupezani:+

  • Salimo 79:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Anthu oyandikana nafe akutitonza,+

      Anthu otizungulira akutinyoza ndi kutiseka.+

  • Salimo 137:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kumeneko, amene anatigwira ukapolo anatiuza kuti tiwaimbire nyimbo,+

      Ndipo otinyozawo anatipempha kuti tiwasangalatse.+ Iwo anati:

      “Tiimbireni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni.”+

  • Luka 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Anthu adzaphedwa ndi lupanga ndiponso kutengedwa ukapolo kupita nawo ku mitundu ina yonse.+ Anthu a mitundu ina adzapondaponda Yerusalemu, kufikira nthawi zoikidwiratu+ za anthu a mitundu inawo zitakwanira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena