Mlaliki 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pa tsiku labwino ukhale munthu wabwino,+ ndipo pa tsiku latsoka uzindikire kuti Mulungu woona anapanga masiku onsewa mofanana,+ ndi cholinga chakuti anthu asadziwe chilichonse chimene chidzachitike pambuyo pawo.+ Yesaya 10:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndidzamutumiza kuti akalimbane ndi mtundu wopanduka,+ ndipo ndidzamulamula kuti akalimbane ndi anthu amene andikwiyitsa. Ndidzamuuza+ kuti akalande zinthu zambiri, akatenge katundu wambiri, ndiponso akapondeponde anthuwo ngati matope a mumsewu.+ Yeremiya 18:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pa nthawi iliyonse imene ndinganene kuti ndizula, kugwetsa ndi kuwononga mtundu uliwonse wa anthu kapena ufumu,+ Amosi 3:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Lipenga la nyanga ya nkhosa likalira mumzinda, kodi anthu sanjenjemera?+ Kodi tsoka likagwa mumzinda si Yehova amene wachititsa?
14 Pa tsiku labwino ukhale munthu wabwino,+ ndipo pa tsiku latsoka uzindikire kuti Mulungu woona anapanga masiku onsewa mofanana,+ ndi cholinga chakuti anthu asadziwe chilichonse chimene chidzachitike pambuyo pawo.+
6 Ndidzamutumiza kuti akalimbane ndi mtundu wopanduka,+ ndipo ndidzamulamula kuti akalimbane ndi anthu amene andikwiyitsa. Ndidzamuuza+ kuti akalande zinthu zambiri, akatenge katundu wambiri, ndiponso akapondeponde anthuwo ngati matope a mumsewu.+
7 Pa nthawi iliyonse imene ndinganene kuti ndizula, kugwetsa ndi kuwononga mtundu uliwonse wa anthu kapena ufumu,+
6 Lipenga la nyanga ya nkhosa likalira mumzinda, kodi anthu sanjenjemera?+ Kodi tsoka likagwa mumzinda si Yehova amene wachititsa?