Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Tsiku lotsatira Aasidodi anadzuka m’mawa kwambiri, ndipo anapeza Dagoni atagwa pansi chafufumimba patsogolo pa likasa la Yehova.+ Zitatero, anatenga Dagoni ndi kumubwezeretsa pamalo ake.+

  • Danieli 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Nebukadinezara anapanga fano lagolide.+ Fanoli linali lalitali mikono* 60 ndipo m’lifupi mwake linali mikono 6. Analiimika m’chigwa cha Dura, m’chigawo cha Babulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena