Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Akanakhala anzeru,+ akanaganizira mozama zimenezi.+

      Akanalingalira kuti ziwathera bwanji.+

  • Miyambo 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mwana wanga, ukamvera mawu anga+ ndi kusunga malamulo anga ngati chuma chamtengo wapatali,+

  • Yesaya 44:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Iwo sadziwa chilichonse+ ndipo samvetsetsa chilichonse+ chifukwa maso awo amatidwa kuti asamaone,+ ndipo mitima yawo ndi yosazindikira zinthu.+

  • Hagai 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsopano Yehova wa makamu wanena kuti, ‘Ganizirani mofatsa zimene mukuchita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena