-
Yesaya 28:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Amenewanso asochera chifukwa cha vinyo. Akuyenda uku ndi uku chifukwa cha chakumwa choledzeretsa. Ansembe ndi aneneri+ asochera chifukwa cha chakumwa choledzeretsa. Asokonezeka chifukwa cha vinyo. Akuyenda uku ndi uku+ chifukwa cha chakumwa choledzeretsa. Sakuonanso bwino ndipo zochita zawo zikusonyeza kuti sakuganiza bwino.
-
-
Mateyu 24:49Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
49 n’kuyamba kumenya akapolo anzake ndi kudya komanso kumwa limodzi ndi zidakwa zenizeni,
-