Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 62:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chipulumutso ndi ulemerero wanga zili mwa Mulungu.+

      Iye ndi thanthwe langa lolimba ndi malo anga othawirako.+

  • Salimo 71:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 M’kamwa mwanga mwadzaza mawu otamanda inu,+

      Ndipo pakamwa panga pakunena za ulemerero wanu tsiku lonse.+

  • Zekariya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ine ndidzamuzungulira ngati mpanda wake wamoto+ ndipo ndidzamudzaza ndi ulemerero wanga,”’ watero Yehova.”+

  • Luka 2:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Maso anga aona kuwala+ kochotsa nsalu yophimba+ mitundu ya anthu+ ndi ulemerero wa anthu anu Aisiraeli.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena