Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 48:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Phiri la Ziyoni limene lili m’dera lakutali la kumpoto,+

      Ndi lokongola chifukwa lili pamalo okwezeka ndi osangalatsa padziko lonse lapansi,+

      Mudzi wa Mfumu Yaikulu.+

  • Salimo 50:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mulungu wawala ali ku Ziyoni,+ mzinda wokongola kwambiri.+

  • Zekariya 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Pa tsiku limenelo, Yehova Mulungu adzapulumutsa nkhosa zake,+ zimene ndi anthu ake.+ Pakuti iwo adzakhala ngati miyala yonyezimira ya pachisoti chachifumu m’dziko lake.+

  • 1 Atesalonika 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kodi chiyembekezo chathu, kapena chimwemwe chathu n’chiyani? Inde, mphoto*+ yathu yoinyadira pamaso pa Ambuye wathu Yesu, pa nthawi ya kukhalapo*+ kwake n’chiyani? Si inu amene kodi?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena