Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komanso nkhumba,+ chifukwa ziboda zake n’zogawanika ndipo zili ndi mpata pakati, koma siibzikula. Ikhale yodetsedwa kwa inu.

  • Deuteronomo 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Musamadyenso nkhumba+ chifukwa ndi ya ziboda zogawanika koma sibzikula. Imeneyi ndi yodetsedwa kwa inu. Musamadye nyama yake ndipo ikafa musamaikhudze.+

  • Yesaya 65:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 amene amakhala pansi kumanda,+ amene amakhala usiku wonse m’tinyumba ta alonda, amene amadya nyama ya nkhumba,+ ndipo m’miphika mwawo muli msuzi wa zinthu zodetsedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena