Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Moyo wathu wakhala ukuyembekeza Yehova.+

      Iye ndi mthandizi wathu ndi chishango chathu.+

  • Salimo 39:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Nanga tsopano, inu Yehova, ine ndikuyembekezera chiyani?

      Chiyembekezo changa chili mwa inu.+

  • Aheberi 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pitirizani kuchita zimenezi kuti musakhale aulesi,+ koma mukhale otsanzira+ anthu amene, mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima, akulandira zinthu zimene Mulungu analonjeza monga cholowa chawo.+

  • 2 Petulo 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Yehova sakuchedwa kukwaniritsa lonjezo lake,+ ngati mmene anthu ena amaonera kuti akuchedwa, koma akuleza nanu mtima, pakuti safuna kuti wina aliyense adzawonongedwe, koma amafuna kuti anthu onse alape.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena