2 Mafumu 18:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Kodi milungu ya Hamati+ ndi Aripadi+ ili kuti? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu,+ Hena,+ ndi Iva?+ Kodi yalanditsa Samariya m’manja mwanga?+ 2 Mafumu 19:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Atentha milungu yawo pamoto, chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga. 2 Mbiri 32:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Anapitiriza kulankhula monyoza+ Mulungu wa Yerusalemu+ mofanana ndi mmene ankanyozera milungu ya mitundu ya anthu a padziko lapansi, yopangidwa ndi manja a anthu.+
34 Kodi milungu ya Hamati+ ndi Aripadi+ ili kuti? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu,+ Hena,+ ndi Iva?+ Kodi yalanditsa Samariya m’manja mwanga?+
18 Atentha milungu yawo pamoto, chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga.
19 Anapitiriza kulankhula monyoza+ Mulungu wa Yerusalemu+ mofanana ndi mmene ankanyozera milungu ya mitundu ya anthu a padziko lapansi, yopangidwa ndi manja a anthu.+