Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa zikondwerero zawo amaimbapo azeze, zoimbira za zingwe, maseche, ndi zitoliro ndipo amamwapo vinyo.+ Koma sayang’ana ntchito ya Yehova, ndipo ntchito ya manja ake saiona.+

  • Yesaya 56:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Tabwerani amuna inu! Dikirani kaye ndikatenge vinyo. Timwe mpaka kuledzera.+ Mawa lidzakhalanso ngati lero, mwinanso kuposa pamenepa.”+

  • Amosi 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Anthu inu mukugona pamipando ya minyanga ya njovu+ ndi kudziwongola pamabedi, ndiponso mukudya nyama ya ana a nkhosa ndi ana amphongo onenepa a ng’ombe zanu.+

  • Luka 17:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 M’masiku amenewo anthu anali kudya, kumwa, amuna anali kukwatira, akazi anali kukwatiwa, kufikira tsiku limene Nowa analowa m’chingalawa, ndipo chigumula chinafika ndi kuwononga anthu onsewo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena