Yobu 34:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Chifukwa asiya kumutsatira,+Ndipo sasamala za njira zake zonse,+ Salimo 19:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Zakumwamba zikulengeza ulemerero wa Mulungu.+Ndipo m’mlengalenga mukufotokoza ntchito ya manja ake.+ Salimo 28:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pakuti iwo salabadira zochita za Yehova,+Kapena ntchito za manja ake.+Mulungu sadzawamanga koma adzawapasula. Salimo 92:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Munthu wopanda nzeru sangadziwe zimenezi,+Ndipo munthu wopusa sangazimvetse.+
27 Chifukwa asiya kumutsatira,+Ndipo sasamala za njira zake zonse,+ Salimo 19:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Zakumwamba zikulengeza ulemerero wa Mulungu.+Ndipo m’mlengalenga mukufotokoza ntchito ya manja ake.+ Salimo 28:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pakuti iwo salabadira zochita za Yehova,+Kapena ntchito za manja ake.+Mulungu sadzawamanga koma adzawapasula. Salimo 92:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Munthu wopanda nzeru sangadziwe zimenezi,+Ndipo munthu wopusa sangazimvetse.+
19 Zakumwamba zikulengeza ulemerero wa Mulungu.+Ndipo m’mlengalenga mukufotokoza ntchito ya manja ake.+
5 Pakuti iwo salabadira zochita za Yehova,+Kapena ntchito za manja ake.+Mulungu sadzawamanga koma adzawapasula.