-
Salimo 8:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Ndikayang’ana kumwamba, ntchito ya zala zanu,+
Mwezi ndi nyenyezi zimene munapanga,+
-
Aroma 1:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Chilengedwere dziko kupita m’tsogolo,+ makhalidwe a Mulungu osaoneka+ ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa, ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu+ wake, zikuonekera m’zinthu zimene anapanga+ moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.+
-
-
-