Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 mwamuna wamphamvu, munthu wankhondo, woweruza, mneneri,+ wowombeza, mwamuna wachikulire,+

  • Yesaya 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 chotero Yehova adzadula mutu+ ndi mchira+ wa Isiraeli. Adzadulanso mphukira ndi udzu* tsiku limodzi.+

  • Ezekieli 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Nthawi idzakwana, tsikulo lidzafika. Wogula asasangalale+ ndipo wogulitsa asalire, pakuti mkwiyo wa Mulungu wayakira khamu lonselo.

  • Hoseya 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Zimene zidzachitikira anthuwo zidzachitikiranso ansembe.+ Ndidzawaimba mlandu onsewa chifukwa cha njira zawo+ ndipo ndidzawabwezera zochita zawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena