Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 54:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pakuti anandilanditsa pa mavuto anga onse,+

      Ndipo diso langa laona adani anga atagonja.+

  • Salimo 59:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu amene wandisonyeza kukoma mtima kosatha ndidzaonana naye maso ndi maso.+

      Mulungu adzachititsa kuti ndione adani anga, adaniwo atagonja.+

  • Yeremiya 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Anthu amene amandizunza achite manyazi+ koma musalole kuti ineyo ndichite manyazi.+ Anthuwo agwidwe ndi mantha aakulu koma musalole kuti ine ndigwidwe ndi mantha aakulu. Agwetsereni tsoka+ ndipo muwaphwanye kuwirikiza kawiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena