Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yembekezera Yehova, ndi kusunga njira zake,+

      Ndipo adzakukweza kuti ulandire dziko lapansi.+

      Pamene oipa akuphedwa, iwe udzaona.+

  • Salimo 59:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu amene wandisonyeza kukoma mtima kosatha ndidzaonana naye maso ndi maso.+

      Mulungu adzachititsa kuti ndione adani anga, adaniwo atagonja.+

  • Salimo 91:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Udzayang’ana ndi maso ako,+

      Ndipo udzaona anthu oipa akulandira chilango.+

  • Salimo 92:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Diso langa lidzayang’ana adani anga atagonja,+

      Makutu anga adzamva za anthu ondiukira, anthu ochita zoipa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena