Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 15:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Koma sanachotse malo okwezeka.+ Anthu anali kufukizabe ndi kupereka nsembe yautsi m’malo okwezekawo. Iye ndiye anamanga chipata chakumtunda cha nyumba ya Yehova.+

  • 2 Mbiri 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iye anamanga chipata chakumtunda+ cha nyumba ya Yehova ndipo pakhoma la Ofeli+ anamangapo zinthu zambiri.

  • Yeremiya 36:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano Baruki anayamba kuwerenga mpukutuwo mokweza pamaso pa anthu onse. Anayamba kuwerenga mawu onse a Yeremiya panyumba ya Yehova. Anachita izi m’chipinda chodyera+ cha Gemariya+ mwana wa Safani+ wokopera Malemba,+ m’bwalo lakumtunda, pakhomo la chipata chatsopano cha nyumba ya Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena