Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iye ali ndi maganizo amodzi, ndani angam’tsutse?+

      Zimene moyo wake umalakalaka amazichita.+

  • Salimo 33:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zolinga za Yehova zidzakhalapo mpaka kalekale.+

      Maganizo a mumtima mwake adzakhalapo ku mibadwomibadwo.+

  • Salimo 40:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Yehova Mulungu wanga, mwatichitira zinthu zambiri zodabwitsa,+

      Ndipo mumatiganizira.+

      Palibe angafanane ndi inu.+

      Ndikafuna kulankhula ndi kunena za zodabwitsazo,

      Zimachuluka kwambiri moti sindingathe kuzifotokoza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena