Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kodi pali chosatheka ndi Yehova?+ Pa nthawi yoikidwiratu ndidzabweranso kwa iwe chaka chamawa. Ndidzabweranso nthawi ngati yomwe ino, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.”

  • Yobu 42:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Ndadziwa kuti inu mumatha kuchita zinthu zonse,+

      Ndipo palibe zimene simungakwanitse.+

  • Luka 1:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Izi zachitika chifukwa zimene Mulungu wanena, sizilephereka.”+

  • Aroma 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 ndipo anali wotsimikiza kuti zimene Mulungu analonjeza anali ndi mphamvu yozichita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena