Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 15:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ku Sefela+ kunali Esitaoli,+ Zora,+ Asina,

  • Yeremiya 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anthu adzabwera kuchokera m’mizinda ya Yuda, m’madera ozungulira Yerusalemu, m’dziko la Benjamini,+ kuchigwa,+ m’dera lamapiri+ komanso kuchokera kum’mwera.*+ Iwo adzabweretsa kunyumba ya Yehova nsembe zopsereza zathunthu,+ nsembe zina,+ nsembe zambewu,+ lubani*+ ndi nsembe zoyamikira.+

  • Yeremiya 33:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Yehova wanena kuti, ‘Ziweto zidzadutsa pansi pa dzanja la munthu woziwerenga+ m’mizinda ya m’madera amapiri, m’mizinda ya m’chigwa,+ m’mizinda ya kum’mwera,+ m’dziko la Benjamini,+ m’madera ozungulira Yerusalemu+ ndi m’mizinda ya Yuda.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena