Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 96:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nenani pakati pa anthu a mitundu ina kuti: “Yehova wakhala mfumu.+

      Dziko lapansi nalonso lakhazikika moti silingagwedezeke.+

      Iye adzaweruzira mitundu ya anthu milandu yawo mwachilungamo.”+

  • Salimo 104:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mwakhazikitsa dziko lapansi pamaziko olimba.+

      Silidzagwedezeka mpaka kalekale, mpaka muyaya.+

  • Salimo 119:90
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  90 Kukhulupirika kwanu kudzakhalapobe ku mibadwomibadwo.+

      Mwakhazikitsa mwamphamvu dziko lapansi, kuti lisagwedezeke.+

  • Mlaliki 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 M’badwo umapita+ ndipo m’badwo wina umabwera,+ koma dziko lapansi lidzakhalapobe mpaka kalekale.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena