15 “Ndipo iye akayamba kubereka ndi kutulutsa ana ngati bango,+ mphepo ya kum’mawa, mphepo ya Yehova idzabwera.+ Mphepo yake ikuchokera kuchipululu ndipo idzaumitsa chitsime chake ndi kuphwetsa kasupe wake.+ Ameneyo adzawononga chuma chimene chikuphatikizapo zinthu zosiririka.+