Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 11:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kodi aliyense amene mulungu wako Kemosi+ wakuchititsa kuti umugonjetse, si amene udzam’gonjetsa? Chotero aliyense amene Yehova Mulungu wathu wam’gonjetsa pamaso pathu ndi amenenso ife tidzam’gonjetsa.+

  • 1 Mafumu 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Panali pa nthawi imeneyi pamene Solomo anamangira Kemosi+ malo okwezeka,+ chinthu chonyansa+ cha Mowabu, paphiri+ lomwe linali patsogolo+ pa Yerusalemu. Anamangiranso Moleki malo okwezeka, yemwe ndi chinthu chonyansa cha ana a Amoni.

  • Yesaya 45:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu adzachita manyazi ndipo onsewo adzanyozeka. Anthu opanga mafano adzayenda monyozeka onse pamodzi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena