Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu akazi amene mukukhala mosatekeseka, njenjemerani! Inu osasamala, chitani mantha! Vulani n’kukhala maliseche, ndipo muvale ziguduli m’chiuno mwanu.+

  • Yeremiya 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pachifukwa chimenechi valani ziguduli,* anthu inu.+ Dzigugudeni pachifuwa ndi kulira mofuula,+ chifukwa mkwiyo woyaka moto wa Yehova sunatichokere.+

  • Yeremiya 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iwe mwana wamkazi wa anthu anga, vala chiguduli*+ ndi kuvimvinizika m’phulusa.+ Lira ngati kuti ukulira maliro a mwana wamwamuna mmodzi yekhayo. Lira mowawidwa mtima+ chifukwa wofunkha adzatiukira modzidzimutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena