Numeri 23:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pakuti pomwe ndili pano ndikutha kuwaona, pamwamba pa matanthwe pano,Ndikuwaona ndithu, pano pamwamba pa mapiri.Akukhala paokhaokha m’mahema awo,+Iwo akudziona kuti ndi osiyana ndi mitundu ina.+ Deuteronomo 33:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Isiraeli adzakhala motetezeka,+Kasupe wa Yakobo adzakhala mosatekeseka,+M’dziko lokhala ndi chakudya ndi vinyo watsopano.+Ndipo kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+ Mika 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Weta anthu ako ndi ndodo yako.+ Weta gulu la nkhosa zomwe ndi cholowa chako, zimene zinali kukhala zokhazokha m’nkhalango pakati pa mitengo ya zipatso.+ Uzilole kuti zikadyere ku Basana ndi ku Giliyadi+ ngati mmene zinali kuchitira masiku akale.+
9 Pakuti pomwe ndili pano ndikutha kuwaona, pamwamba pa matanthwe pano,Ndikuwaona ndithu, pano pamwamba pa mapiri.Akukhala paokhaokha m’mahema awo,+Iwo akudziona kuti ndi osiyana ndi mitundu ina.+
28 Isiraeli adzakhala motetezeka,+Kasupe wa Yakobo adzakhala mosatekeseka,+M’dziko lokhala ndi chakudya ndi vinyo watsopano.+Ndipo kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+
14 Weta anthu ako ndi ndodo yako.+ Weta gulu la nkhosa zomwe ndi cholowa chako, zimene zinali kukhala zokhazokha m’nkhalango pakati pa mitengo ya zipatso.+ Uzilole kuti zikadyere ku Basana ndi ku Giliyadi+ ngati mmene zinali kuchitira masiku akale.+