Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 13:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndi mauta awo, adzaphwanyaphwanya ngakhale anyamata awo.+ Iwo sadzamvera chisoni zipatso za m’mimba.+ Diso lawo silidzamvera chisoni ana aamuna.

  • Yeremiya 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti imfa yatilowera m’nyumba kudzera m’mawindo. Yalowa munsanja zathu zokhalamo kuti mumsewu musapezeke mwana aliyense ndiponso kuti anyamata asapezeke m’mabwalo a mzinda.’+

  • Yeremiya 49:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Choncho anyamata ake adzaphedwa m’mabwalo ake, ndipo amuna ake ankhondo adzawakhalitsa chete pa tsiku limenelo,”+ watero Yehova wa makamu.

  • Yeremiya 51:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Muwaphe ndi kusiya mitembo yawo ili paliponse m’dziko la Akasidi.+ Muwasiye mutawabaya m’misewu ya m’dzikolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena