Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chotero Afilisiti anamenyadi nkhondo, ndipo Aisiraeli anagonja+ moti aliyense wa iwo anayamba kuthawira kuhema wake.+ Ndipo amene anaphedwa anali ochuluka kwambiri.+ Panaphedwa amuna oyenda pansi a Isiraeli okwanira 30,000.+

  • Salimo 78:60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 Pamapeto pake anasiya chihema chopatulika cha ku Silo,+

      Hema limene anali kukhalamo pakati pa anthu ochokera kufumbi.+

  • Yeremiya 26:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 pamenepo ine ndidzachititsa nyumba iyi kukhala ngati nyumba ya ku Silo.+ Ndipo mzinda uwu ndidzausandutsa chinthu chotembereredwa pakati pa anthu a mitundu yonse ya padziko lapansi.’”’”+

  • Maliro 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+

      Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+

      Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena