1 Samueli 4:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chotero Afilisiti anamenyadi nkhondo, ndipo Aisiraeli anagonja+ moti aliyense wa iwo anayamba kuthawira kuhema wake.+ Ndipo amene anaphedwa anali ochuluka kwambiri.+ Panaphedwa amuna oyenda pansi a Isiraeli okwanira 30,000.+ Salimo 78:60 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 60 Pamapeto pake anasiya chihema chopatulika cha ku Silo,+Hema limene anali kukhalamo pakati pa anthu ochokera kufumbi.+ Yeremiya 26:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 pamenepo ine ndidzachititsa nyumba iyi kukhala ngati nyumba ya ku Silo.+ Ndipo mzinda uwu ndidzausandutsa chinthu chotembereredwa pakati pa anthu a mitundu yonse ya padziko lapansi.’”’”+ Maliro 2:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+
10 Chotero Afilisiti anamenyadi nkhondo, ndipo Aisiraeli anagonja+ moti aliyense wa iwo anayamba kuthawira kuhema wake.+ Ndipo amene anaphedwa anali ochuluka kwambiri.+ Panaphedwa amuna oyenda pansi a Isiraeli okwanira 30,000.+
60 Pamapeto pake anasiya chihema chopatulika cha ku Silo,+Hema limene anali kukhalamo pakati pa anthu ochokera kufumbi.+
6 pamenepo ine ndidzachititsa nyumba iyi kukhala ngati nyumba ya ku Silo.+ Ndipo mzinda uwu ndidzausandutsa chinthu chotembereredwa pakati pa anthu a mitundu yonse ya padziko lapansi.’”’”+
7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+