Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 8:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mahatchi ake akumveka kupuma mwawefuwefu ali ku Dani.+ Dziko lonse layamba kugwedezeka chifukwa cha phokoso la kulira kwa mahatchi ake amphongo.+ Adani akubwera kudzawononga dziko ndi zonse zokhala mmenemo, mzinda ndi onse okhala mmenemo.”

  • Maliro 2:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Munaitana+ anthu kuchokera kumalo onse ozungulira, kumene akukhala monga alendo.

      Pa tsiku la mkwiyo wa Yehova panalibe wothawa kapena wopulumuka.+

      Ana onse athanzi amene ndinabereka ndi kuwalera, mdani wanga anawapha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena