Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 10:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Yehu anakumana ndi abale+ ake a Ahaziya+ mfumu ya Yuda. Atawafunsa kuti, “Ndinu ndani?” iwo anayankha kuti: “Ndife abale ake a Ahaziya. Tikupita kukaona ngati ana a mfumu ndi ana a mfumukazi ali bwino.”

  • 2 Mafumu 24:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Patapita nthawi, Yehoyakini mfumu ya Yuda anatuluka n’kupita kwa mfumu ya Babulo+ pamodzi ndi mayi ake,+ atumiki ake, akalonga ake, ndi nduna za panyumba yake, ndipo mfumu ya Babuloyo inam’tengera Yehoyakini ku ukapolo m’chaka cha 8+ cha ufumu wake.

  • Yeremiya 22:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iwe ndi mayi ako+ amene anakubereka, ndidzakuponyani kudziko lina limene anthu inu simunabadwireko ndipo mudzafera kumeneko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena