Yeremiya 8:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Ndasweka mtima+ chifukwa cha kuwonongeka+ kwa mwana wamkazi wa anthu anga. Ndine wachisoni. Ndadabwa kwambiri.+ Maliro 1:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Yehova wandichotsera anthu anga onse amphamvu+ ndi kuwakankhira pambali.Wandiitanitsira msonkhano kuti athyolethyole anyamata anga.+Yehova wapondaponda moponderamo mphesa+ mwa namwali, mwana wamkazi wa Yuda.+
21 Ndasweka mtima+ chifukwa cha kuwonongeka+ kwa mwana wamkazi wa anthu anga. Ndine wachisoni. Ndadabwa kwambiri.+
15 Yehova wandichotsera anthu anga onse amphamvu+ ndi kuwakankhira pambali.Wandiitanitsira msonkhano kuti athyolethyole anyamata anga.+Yehova wapondaponda moponderamo mphesa+ mwa namwali, mwana wamkazi wa Yuda.+