Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Tsopano anthu amene ndi ana aang’ono poyerekeza ndi ine,+

      Akundiseka.+

      Anthu amene abambo awo sindikanalola

      Kuwaika pamodzi ndi agalu oweta nkhosa zanga.

  • Salimo 44:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwatisandutsa chitonzo kwa anthu oyandikana nafe,+

      Mwatisandutsa chinthu chonyozeka ndi choseketsa kwa onse otizungulira.+

  • Yeremiya 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mwandidabwitsa inu Yehova, ndipo ndadabwa. Mwagwiritsa ntchito mphamvu zanu pa ine ndipo mwapambana.+ Ndakhala chinthu choseketsa tsiku lonse. Aliyense akungondinyoza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena