Yobu 12:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ine ndakhala chinthu choseketsa kwa anthu anzanga,+Ndakhala munthu woitana kwa Mulungu kuti amuyankhe.+Munthu wolungama ndi wosalakwa wakhala choseketsa. Salimo 22:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Anthu onse ondiona amandinyodola.+Iwo amandinyogodola ndi pakamwa pawo, ndipo amapukusa mitu yawo mondinyoza.+ Iwo amati: Yeremiya 15:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tsoka ine,+ chifukwa inu mayi anga munabereka ine munthu amene nthawi zonse ndimakangana ndipo ndimalimbana ndi dziko lonse.+ Sindinapereke ngongole komanso sanandikongoze kalikonse, koma anthu onse akunditemberera.+ Maliro 3:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndakhala chinthu choseketsa+ kwa anthu onse odana nane, ndipo amandiimba m’nyimbo yawo tsiku lonse.+ Machitidwe 17:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Ndiyeno anthuwo atamva za kuuka kwa akufa, ena anayamba kuseka monyodola,+ pamene ena anati: “Chabwino, udzatiuzenso zimenezi nthawi ina.”
4 Ine ndakhala chinthu choseketsa kwa anthu anzanga,+Ndakhala munthu woitana kwa Mulungu kuti amuyankhe.+Munthu wolungama ndi wosalakwa wakhala choseketsa.
7 Anthu onse ondiona amandinyodola.+Iwo amandinyogodola ndi pakamwa pawo, ndipo amapukusa mitu yawo mondinyoza.+ Iwo amati:
10 Tsoka ine,+ chifukwa inu mayi anga munabereka ine munthu amene nthawi zonse ndimakangana ndipo ndimalimbana ndi dziko lonse.+ Sindinapereke ngongole komanso sanandikongoze kalikonse, koma anthu onse akunditemberera.+
14 Ndakhala chinthu choseketsa+ kwa anthu onse odana nane, ndipo amandiimba m’nyimbo yawo tsiku lonse.+
32 Ndiyeno anthuwo atamva za kuuka kwa akufa, ena anayamba kuseka monyodola,+ pamene ena anati: “Chabwino, udzatiuzenso zimenezi nthawi ina.”