Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Tsopano ine ndakhala mutu wa nyimbo yawo,+

      Ndipo kwa iwo ndine chinthu choseketsa.+

  • Salimo 69:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthu okhala kuchipata anayamba kundidera nkhawa,+

      Ndipo anthu amene anali kumwa zakumwa zoledzeretsa anali kundinena mu nyimbo zawo.+

  • Salimo 137:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kumeneko, amene anatigwira ukapolo anatiuza kuti tiwaimbire nyimbo,+

      Ndipo otinyozawo anatipempha kuti tiwasangalatse.+ Iwo anati:

      “Tiimbireni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena