Yeremiya 38:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Inu mbuyanga mfumu, zimene anthu awa achitira mneneri Yeremiya ndi zoipa, chifukwa amuponya m’chitsime, ndipo afera momwemo+ chifukwa cha njala,+ pakuti mkate watheratu mumzindawu.” Yeremiya 52:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 M’mwezi wachinayi, pa tsiku la 9,+ njala inafika poipa kwambiri mumzindawo, ndipo anthu a m’dzikolo analibiretu chakudya.+ Maliro 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Iwo anali kufunsa amayi awo kuti: “Kodi chakudya ndi vinyo zili kuti?”+Anali kufunsa chifukwa anali kukomoka m’mabwalo a mzinda ndi kugona pansi ngati anthu ophedwa,Ndiponso chifukwa moyo wawo unali kukhuthukira pachifuwa cha amayi awo. Maliro 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Lilime la ana oyamwa lamamatira kummero chifukwa cha ludzu.+Ana apempha chakudya+ koma palibe amene akuwapatsa.+
9 “Inu mbuyanga mfumu, zimene anthu awa achitira mneneri Yeremiya ndi zoipa, chifukwa amuponya m’chitsime, ndipo afera momwemo+ chifukwa cha njala,+ pakuti mkate watheratu mumzindawu.”
6 M’mwezi wachinayi, pa tsiku la 9,+ njala inafika poipa kwambiri mumzindawo, ndipo anthu a m’dzikolo analibiretu chakudya.+
12 Iwo anali kufunsa amayi awo kuti: “Kodi chakudya ndi vinyo zili kuti?”+Anali kufunsa chifukwa anali kukomoka m’mabwalo a mzinda ndi kugona pansi ngati anthu ophedwa,Ndiponso chifukwa moyo wawo unali kukhuthukira pachifuwa cha amayi awo.
4 Lilime la ana oyamwa lamamatira kummero chifukwa cha ludzu.+Ana apempha chakudya+ koma palibe amene akuwapatsa.+