Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 51:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pa ana onse amene iye anabereka, palibe ndi mmodzi yemwe+ amene anali kutsogolera mayiyo poyenda. Pa ana onse amene iye analera, palibe ndi mmodzi yemwe amene anagwira dzanja lake.+

  • Yeremiya 30:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Achigololo onse amene anali kukukonda kwambiri akuiwala.+ Iwo sakukufunafunanso. Ndakumenya ndi mkwapulo+ ngati mdani ndipo ndakulanga ngati munthu wankhanza+ chifukwa cha kuchuluka kwa zolakwa zako.+ Machimo ako achuluka kwambiri.+

  • Maliro 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Zovala+ zake ndi zodetsedwa. Iye sanaganizire za tsogolo+ lake.

      Wagwa modabwitsa ndipo alibe womutonthoza.+

      Inu Yehova, onani kusautsika+ kwanga, pakuti mdani wanga akudzitukumula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena