Deuteronomo 28:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Udzalonjeza kukwatira mkazi koma mwamuna wina adzamugwirira.+ Udzamanga nyumba koma sudzakhalamo.+ Udzabzala mitengo ya mpesa koma sudzadya zipatso zake.+ Maliro 2:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Yehova wachita zimene anali kuganiza.+ Wakwaniritsa zimene ananena,+Zimene analamula kalekale.+ Wapasula zinthu ndipo sanamve chisoni.+Wachititsa adani ako kusangalala+ chifukwa cha zimene zakuchitikira. Wakweza nyanga ya adani+ ako. Maliro 3:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Mwadzitchinga ndi mkwiyo wanu kuti tisakufikireni+ ndipo mukupitiriza kutithamangitsa.+ Mwapha anthu mopanda chisoni.+
30 Udzalonjeza kukwatira mkazi koma mwamuna wina adzamugwirira.+ Udzamanga nyumba koma sudzakhalamo.+ Udzabzala mitengo ya mpesa koma sudzadya zipatso zake.+
17 Yehova wachita zimene anali kuganiza.+ Wakwaniritsa zimene ananena,+Zimene analamula kalekale.+ Wapasula zinthu ndipo sanamve chisoni.+Wachititsa adani ako kusangalala+ chifukwa cha zimene zakuchitikira. Wakweza nyanga ya adani+ ako.
43 Mwadzitchinga ndi mkwiyo wanu kuti tisakufikireni+ ndipo mukupitiriza kutithamangitsa.+ Mwapha anthu mopanda chisoni.+