Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova ataona zimenezi anayamba kuwanyoza,+

      Chifukwa chakuti ana ake aamuna ndi aakaziwo anam’sautsa.

  • Salimo 78:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Mulungu anamva+ ndipo anakwiya kwambiri.+

      Chotero ananyansidwa kwambiri ndi Isiraeli.+

  • Salimo 106:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Mkwiyo wa Yehova unayamba kuyakira anthu ake,+

      Ndipo iye ananyansidwa ndi cholowa chake.+

  • Yeremiya 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Iwe Yerusalemu, mvera chilango+ kuti ndisatembenuke ndi kukufulatira chifukwa chonyansidwa nawe,+ kuti ndisakusandutse bwinja, dziko lopanda munthu aliyense wokhalamo.”+

  • Yeremiya 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Wokondedwa wangayo, amene ndi cholowa changa, wakhala ngati mkango kwa ine m’nkhalango ndipo wandibangulira. N’chifukwa chake ndadana naye.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena