Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Unyamule katunduyo paphewa iwo akuona, ndipo utulutse katunduyo kuli mdima. Uphimbe nkhope yako kuti usaone dziko chifukwa ndakuika kuti ukhale chizindikiro+ kwa nyumba ya Isiraeli.”+

  • Ezekieli 24:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ezekieli wakhala chizindikiro cholosera zam’tsogolo.+ Mudzachita zonse zimene iye wachita. Mudzachita zimenezo tsoka lanu likadzafika,+ ndipo mudzadziwa kuti ine ndine Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena