Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 40:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mkwiyo wako wosefukira utuluke,+

      Ndipo uone aliyense wodzikweza n’kumutsitsa.

  • Salimo 73:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithudi, mwawaimika pamalo oterera.+

      Mwawagwetsa kuti awonongeke.+

  • Salimo 147:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova amathandiza anthu ofatsa,+

      Koma anthu oipa amawagwetsera pansi.+

  • Yesaya 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Koma adzakutsitsira ku Manda,+ pansi penipeni pa dzenje.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena