Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 28:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 ine ndikubweretsera alendo,+ anthu ankhanza a mitundu ina.+ Iwo adzasolola lupanga n’kuwononga chilichonse chokongola chimene unapeza chifukwa cha nzeru zako, ndipo adzaipitsa ulemerero wako wonyezimira.+

  • Habakuku 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ine ndikuutsa Akasidi,+ mtundu waukali ndi waphuma umene ukupita kumalo otakasuka a padziko lapansi kukatenga malo amene si awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena