Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 48:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Mumzinda wa Mulungu wathu,+ m’phiri lake loyera.+

  • Ezekieli 48:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 “Kuzungulira mzindawo pakhale mtunda wokwana mikono 18,000. Kuyambira pa tsiku limenelo, dzina la mzindawo lidzakhala lakuti, Yehova Ali Kumeneko.”+

  • Zefaniya 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova wachotsa zigamulo zake pa iwe.+ Watembenuza ndi kubweza mdani wako.+ Mfumu ya Isiraeli, Yehova, ali pakati pa anthu ako+ ndipo sudzaopanso kuti tsoka likugwera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena