Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mudzawabisa m’malo otetezeka pafupi ndi inu,+

      Kuwachotsa pamaso pa anthu amene asonkhana pamodzi kuti awachitire chiwembu.+

      Mudzawabisa mumsasa wanu kwa anthu ofuna kukangana nawo.+

  • Salimo 90:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 90 Inu Yehova, ndinudi malo athu okhalamo+

      Ku mibadwomibadwo.+

  • Salimo 91:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Popeza wanena kuti: “Yehova ndiye pothawirapo panga,”+

      Wapanga Wam’mwambamwamba kukhala malo ako okhalamo.+

  • Miyambo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba.+ Wolungama amathawira mmenemo ndipo amatetezedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena