Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo mngelo wa Yehova anauza Eliya kuti: “Tsika upite naye limodzi, usamuope.”+ Choncho Eliya ananyamuka n’kupita pamodzi ndi mtsogoleri uja kwa mfumu.

  • Miyambo 29:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kuopa anthu n’kumene kumatchera msampha,+ koma wokhulupirira Yehova adzatetezedwa.+

  • Yeremiya 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Koma iwe umange m’chiuno+ ndipo upite kukawauza zonse zimene ndikulamule kuti ukawauze. Usagwidwe ndi mantha chifukwa cha iwo,+ kuopera kuti ndingakuchititse kugwidwa ndi mantha pamaso pawo.

  • Luka 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komanso ndikukuuzani ndithu, mabwenzi anga,+ Musamaope amene amapha thupi lokha, amene sangathe kuchita zoposa pamenepa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena