Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 9:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Zokolola za m’dzikoli zachulukira+ mafumu+ amene mwatiikira chifukwa cha machimo athu.+ Iwo akulamulira matupi athu komanso ziweto zathu mmene akufunira, ndipo tili pamavuto aakulu.+

  • Ezekieli 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ngakhale kuti anatambasula dzanja lake+ povomereza lumbiro, iye wanyoza lumbiro+ limenelo mwa kuphwanya pangano. Iye wachita zinthu zonsezi ndipo sadzapulumuka.”’+

  • Ezekieli 21:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Chotsa nduwira* ndipo vula chisoti chachifumu.+ Zinthu zasintha tsopano.+ Kweza munthu wotsika+ ndipo tsitsa munthu wokwezeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena