Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Atatero, Farao anavula mphete yake yachifumu+ kudzanja lake, n’kuiveka kudzanja la Yosefe. Anamuvekanso malaya amtengo wapatali, ndi tcheni chagolide m’khosi mwake.+

  • 1 Samueli 17:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pamenepo amuna a Isiraeli anayamba kunena kuti: “Mukumuona mwamuna amene akubwerayu? Iye akubwera kudzatonza+ Isiraeli. Munthu amene angamukanthe ndi kumupha, mfumu idzam’patsa chuma chochuluka ndi kum’patsanso mwana wake wamkazi.+ Komanso, mfumu idzamasula nyumba ya bambo ake a munthuyo kuti isamapereke chilichonse mwa zinthu zimene Aisiraeli ayenera kupereka kwa mfumu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena