Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 2:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 “Pambuyo panu padzabwera ufumu wina+ wotsikirapo kwa inu.+ Kenako padzabweranso ufumu wina wachitatu, wamkuwa, umene udzalamulira dziko lonse lapansi.+

  • Danieli 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamene ndinali kuganizira zimenezi, ndinangoona mbuzi yamphongo+ ikuchokera kolowera dzuwa kudutsa padziko lonse lapansi koma sinali kukhudza pansi. Pakati pa maso a mbuziyo panali nyanga yoonekera patali.+

  • Danieli 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Choncho iye anandiuza kuti:

      “Kodi ukudziwadi kuti n’chifukwa chiyani ndabwera kwa iwe? Tsopano ndibwerera kuti ndikamenyane ndi kalonga wa Perisiya.+ Pamene ndikupita, nayenso kalonga wa Girisi akubwera.+

  • Danieli 11:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Ndiyeno mfumu yamphamvu idzauka ndi kulamulira ndi mphamvu zazikulu,+ ndipo idzachitadi zofuna zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena